Gayana Sharifov amaphunzira m'mwezi wa 5 wa mimba kuti mwana wake woyamba alibe mphamvu chifukwa cha kusowa kwa impso ndi chikhodzodzo.Iye ndi mwamuna wake mokhulupilika amaika mkhalidwe umenewu m’manja mwa Mulungu ndipo akusimba mmene Mulungu wakhala akuwatsogolela ndi kuwalimbikitsa ndi kuwapatsa zokumana nazo zabwino kwambili.
Siyani Comment